Oweruza 7:20 BL92

20 Ndi magulu atatuwo anaomba malipenga, naswa mbiyazo, nagwira miuni ndi dzanja lao lamanzere, ndi malipenga m'dzanja lao lamanja kuwaomba; ndipo anapfuula, Lupanga la Yehova ndi la Gideoni.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 7

Onani Oweruza 7:20 nkhani