Oweruza 7:22 BL92

22 Ndipo mazana atatuwa anaomba malipenga, ndipo Yehova anakanthanitsa yense mnzace ndi lupanga m'misasa monse; ndi a m'misasa anathawa mpaka ku Betesita ku Zerera, mpaka ku malire a Abelemehola pa Tabati.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 7

Onani Oweruza 7:22 nkhani