Oweruza 7:23 BL92

23 Pamenepo anthu a Israyeli analalikidwa kucokera ku Nafitali, ndi ku Aseri, ndi ku Manase yense, nalondola Amidyani.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 7

Onani Oweruza 7:23 nkhani