Oweruza 7:8 BL92

8 Pamenepo anthu anatenga kamba m'dzanja lao, ndi malipenga ao; ndipo anauza amuna onse a Israyeli amuke, yense kuhema kwace; koma anaimika amuna mazana atatuwo; ndipo misasa ya Midyani inali kunsi kwace m'cigwa.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 7

Onani Oweruza 7:8 nkhani