Oweruza 8:20 BL92

20 Nati kwa Yeteri mwana wace woyamba, Tauka, nuwaphe. Koma mnyamatayo sanasolola lupanga lace; pakuti anaopa, pokhala anali mnyamata.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 8

Onani Oweruza 8:20 nkhani