Oweruza 8:21 BL92

21 Pamenepo Zeba ndi Tsalimuna anati, Tauka iwe mwini nutigwere; pakuti monga munthu momwemo mphamvu yace. Ndipo Gideoni anauka nawapha Zeba ndi Tsalimuna, nalanda mphande zinali kukhosi kwa ngamila zao.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 8

Onani Oweruza 8:21 nkhani