Oweruza 8:22 BL92

22 Pamenepo anthu a Israyeli anati kwa Gideoni, Mutilamulire ndi inu, ndi mwana wanu, ndi mdzukulu wanu, pakuti mwatipulumutsa m'dzanja la Amidyani.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 8

Onani Oweruza 8:22 nkhani