Oweruza 8:27 BL92

27 Ndipo Gideoni anawapanga fano, naliika m'mudzi mwace, ndiwo Ofira; ndi Israyeli yense analitsata kuligwadira pomwepo; ndipo linakhala kwa Gideoni ndi nyumba yace ngati msampha.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 8

Onani Oweruza 8:27 nkhani