Oweruza 9:23 BL92

23 Mulungu anatumiza mzimu woipa pakati pa Abimeleki ndi eni ace a ku Sekemu; ndi eni ace a ku Sekemu anamcitira Abimeleki mosakhulupirika;

Werengani mutu wathunthu Oweruza 9

Onani Oweruza 9:23 nkhani