Yohane 3:2 BL92

2 Iyeyu anadza kwa Yesu usiku, nati kwa iye, Rabi, tidziwa kuti Inu ndinu mphunzitsi wocokera kwa Mulungu; pakuti palibe munthu akhoza kucita zizindikilo zimene inu mucita, ngati Mulungu sakhala naye,

Werengani mutu wathunthu Yohane 3

Onani Yohane 3:2 nkhani