26 Ndipo Yerobiamu mwana wa Nebati M-efrati wa ku Zereda mnyamata wa Solomo, dzina la amace ndiye Zeruwa, mkazi wamasiye, iyenso anakweza dzanja lace pa mfumu.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 11
Onani 1 Mafumu 11:26 nkhani