36 Ndipo ndidzamninkha mwana wace pfuko limodzi, kuti Davide mtumiki wanga akhale cikhalire ndi nyali pamaso panga m'Yerusalemu, mudzi umene ndinadzisankhira kuikapo dzina langa.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 11
Onani 1 Mafumu 11:36 nkhani