1 Mafumu 14:10 BL92

10 cifukwa cace, taona, ndidzafikitsa coipa pa nyumba ya Yerobiamu, ndi kugurula mwana wamwamuna yense wa Yerobiamu womangika ndi womasuka m'Israyeli, ndipo ndidzacotsa psiti nyumba yonse ya Yerobiamu, monga munthu acotsa ndowe kufikira idatha yonse.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 14

Onani 1 Mafumu 14:10 nkhani