3 Nayenda iye m'zoipa zonse za atate wace, zimene iye adacita asanalowe ufumu Abiyayo; ndipo mtima wace sunali wangwiro ndi Yehova Mulungu wace monga mtima wa Davide kholo lace.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 15
Onani 1 Mafumu 15:3 nkhani