40 Ndipo Eliya anati kwa iwo, Gwirani aneneri a Baala, asapulumuke ndi mmodzi yense. Nawagwira, ndipo Eliya ana pita nao ku mtsinje wa Kisoni, nawapha pamenepo.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 18
Onani 1 Mafumu 18:40 nkhani