1 Mafumu 22:24 BL92

24 Pamenepo Zedekiya mwana wa Kenana anasendera, napanda Mikaya patsaya, nati, Mzimu wa Yehova wandicokera bwanji, kulankhula ndi iwe?

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 22

Onani 1 Mafumu 22:24 nkhani