1 Mafumu 6:27 BL92

27 Ndipo anaika akerubiwo m'cipinda ca m'katimo, ndi mapiko a akerubiwo anatambasuka kotero kuti phiko lace la kerubi mmodzi linajima ku khoma limodzi, ndipo phiko la kerubi wina linajima khoma lina, ndi mapiko ao anagundana pakati pa nyumba.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 6

Onani 1 Mafumu 6:27 nkhani