1 Mafumu 8:21 BL92

21 Ndipo ndakonzera malo likasalo, m'mene muli cipangano ca Yehova, cimene anapangana ndi makolo athu pamene anawaturutsa m'dziko la Aigupto.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8

Onani 1 Mafumu 8:21 nkhani