Deuteronomo 23:20 BL92

20 Mukongoletse mlendo mopindulitsa; koma mbale wanu musamamkongoletsa mopindulitsa, kuti Yehova Mulungu wanu akudalitseni mwa zonse muzigwira ndi dzanja lanu, m'dziko limene mulowamo kulilandira.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 23

Onani Deuteronomo 23:20 nkhani