Deuteronomo 25:7 BL92

7 Ndipo ngati mwamunayo safuna kutenga mkazi wa mbale wace, mkazi wa mbale waceyo azikwera kumka kucipata, kwa akuru, ndi kuti, Mbale wa mwamuna wanga akana kuutsira mbale wace dzina m'Israyeli; safuna kundicitira ine zoyenera mbale wa mwamuna.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 25

Onani Deuteronomo 25:7 nkhani