Deuteronomo 32:21 BL92

21 Anautsa nsanje yanga ndi cinthu cosati Mulungu;Anautsa mkwiyo wanga om zopanda pace zao.Ndidzautsa nsanje yao ndi iwo osakhala mtundu wa anthu;Ndidzautsa mkwiyo wao ndi mtundu wa anthu opusa.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 32

Onani Deuteronomo 32:21 nkhani