Deuteronomo 34:4 BL92

4 Ndipo Yehova anati kwa iye, Si ili dziko ndinalumbirira Abrahamu, Isake, ndi Yakobo, ndi kuti, Ndidzalipereka kwa mbeu zako. Ndinakuonetsa ili m'maso, koma sudzaolokako.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 34

Onani Deuteronomo 34:4 nkhani