Deuteronomo 5:33 BL92

33 Muziyenda m'njira yonse imene Yehova Mulungu wanu anakulamulirani, kuti mukakhale ndi moyo, ndi kuti cikukomereni, ndi kuti masiku anu acuruke m'dziko limene mudzakhala nalo lanu lanu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 5

Onani Deuteronomo 5:33 nkhani