Deuteronomo 6:10 BL92

10 Ndipo kudzakhala, Yehova Mulungu wanu atakulowetsani m'dziko limene analumbirira makolo anu, Abrahamu, Isake, ndi Yakobo, kuti adzakupatsani ili; midzi yaikuru ndi yokoma, imene simunaimanga;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 6

Onani Deuteronomo 6:10 nkhani