Deuteronomo 7:6 BL92

6 Pakuti inu ndinu mtundu wa anthu wopatulika wa Yehova Mulungu wanu; Yehova Mulungu wanu anakusankhani, mukhale mtundu wa pa wokha wa iye yekha, mwa mitundu yonse ya anthu akukhala pa nkhope ya dziko.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 7

Onani Deuteronomo 7:6 nkhani