Oweruza 1:13 BL92

13 Ndipo Otiniyeli, mwana wa Kenazi mng'ono wa Kalebi anaulanda, ndipo anampatsa Akisa mwana wace wamkazi akhale mkazi wace.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 1

Onani Oweruza 1:13 nkhani