Oweruza 11:36 BL92

36 Ndipo anati kwa iye, Atate wanga, mwamtsegulira Yehova pakamwa panu, mundicitire ine monga umo mudaturutsa mau pakamwa panu; popeza Yehova anakucitirani inu cilango pa adani anu, pa ana a Amoni.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 11

Onani Oweruza 11:36 nkhani