Oweruza 11:8 BL92

8 Ndipo akuru a Gileadi ananena ndi Yefita, Cifukwa cace cakuti takubwerera tsopano ndico kuti umuke nafe ndi kucita nkhondo ndi ana a Amoni, nudzakhala mkuru wathu wa pa onse okhala m'Gileadi.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 11

Onani Oweruza 11:8 nkhani