Oweruza 21:23 BL92

23 Nacita cotere ana a Benjamini, nadzitengera akazi monga mwa kuwerenga kwao, a obvina aja, amene anawatenga mwacifwamba; namuka iwo nabwerera ku colowa cao, namanga midzi, nakhalamo.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 21

Onani Oweruza 21:23 nkhani