Yoswa 1:9 BL92

9 Kodi sindinakulamulira iwe? Khala wamphamvu, nulimbike mtima, usaope, kapena kutenga nkhawa, pakuti Yehova Mulungu wako ali ndi iwe kuli konse umukako.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 1

Onani Yoswa 1:9 nkhani