Yoswa 13:30 BL92

30 Ndipo malire ao anayambira ku Mahanaimu, Basana lonse, ufumu wonse wa Ogi mfumu ya ku Basana, ndi midzi yonse ya Yairi, yokhala m'Basana, midzi makumi asanu ndi limodzi;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 13

Onani Yoswa 13:30 nkhani