Yoswa 17:15 BL92

15 Ndipo Yoswa ananena nao, Ngati muli anthu aunyinji, kwerani kuli mitengoko, ndi kudziswera minda m'dziko la Aperizi ndi la Arefai; akakuceperani malo ku phiri la Efraimu.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 17

Onani Yoswa 17:15 nkhani