3 Ndipo mfumu ya Yeriko inatuma wina kwa Rahabi, ndi kuti, Turutsa amunawo anafika kwanu, amene analowa m'nyumba mwako; popeza anadzera kulizonda dziko lonse.
Werengani mutu wathunthu Yoswa 2
Onani Yoswa 2:3 nkhani