Yoswa 23:16 BL92

16 Mukalakwira cipangano ca Yehova Mulungu wanu cimene analamulira inu ndi kumuka ndi kutumikira milungu yina ndi kuigwadira, mkwiyo wa Mulungu udzayakira inu, nimudzatayika msanga m'dziko lokomali anakupatsani.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 23

Onani Yoswa 23:16 nkhani