Yoswa 24:17 BL92

17 pakuti Yehova Mulungu wathu ndi iye amene anatikweza kutiturutsa m'dziko la Aigupto ku nyumba ya akapolo, nacita zodabwiza zazikuruzo pamaso pathu, natisunga m'njira monse tidayendamo, ndi pakati pa anthu onse amene tinapita pakati pao;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 24

Onani Yoswa 24:17 nkhani