Yoswa 24:2 BL92

2 Ndipo Yoswa ananena ndi anthu onse, Atero Yehova Mulungu wa Israyeli, Kale lija makolo anu anakhala tsidya lija la mtsinje, ndiye Tera, atate wa Abrahamu ndi atate wa Nahori; natumikira milungu yina iwowa.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 24

Onani Yoswa 24:2 nkhani