Yoswa 3:4 BL92

4 Koma pakhale dera pakati pa inu ndi ilo, monga mikono zikwi ziwiri poliyesa; musaliyandikire, kuti mudziwe njira imene muziyendamo; popeza simunapita njirayi kufikira lero.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 3

Onani Yoswa 3:4 nkhani