Yoswa 4:7 BL92

7 munene nao, Cifukwa madzi a Yordano anadulidwa patsogolo pa likasa la cipangano ca Yehova; muja lidaoloka Yordano, madzi a Yordano anadulidwa; ndipo miyala iyi idzakhala cikumbutso ca ana a Israyeli cikhalire.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 4

Onani Yoswa 4:7 nkhani