Yoswa 6:15 BL92

15 Ndipo kunali, tsiku lacisanu ndi ciwiri analawira mamawa, mbandakuca, nazungulira mudzi mommuja kasanu ndi kawiri; koma tsiku lijalo anazungulira mudzi kasanu ndi kawiri.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 6

Onani Yoswa 6:15 nkhani