Yoswa 6:6 BL92

6 Ndipo Yoswa mwana wa Nuni anaitana ansembe, nanena nao, Senzani likasa la cipangano, ndi ansembe asanu ndi awiri anyamule mphalasa zisanu ndi ziwiri zanyanga za nkhosa zamphongo, kutsogolera nazo likasa la Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 6

Onani Yoswa 6:6 nkhani