Yoswa 9:13 BL92

13 ndi matumba a vinyo awa tinawadzaza akali atsopano; ndipo taonani, ang'ambika; ndi malaya athu awa ndi nsapato zathu zatha, cifukwa ca ulendo wocokera kutali ndithu.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 9

Onani Yoswa 9:13 nkhani