5 Ndipo anabala mwana wamwamuna, amene adzaweruza mitundu yonse ndi ndodo yacitsulo: ndipo anakwatulidwa mwana wace amuke kwa Mulungu, ndi ku mpando wacifumu wace.
Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 12
Onani Cibvumbulutso 12:5 nkhani