2 Nafika ku Yerusalemu ndi ulendo wace waukulu, ndi ngamila zakunyamula zonunkhira, ndi golidi wambiri, ndi timiyala ta mtengo wapatali; ndipo atafika kwa Solomo anakamba naye zonse za m'mtima mwace.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 10
Onani 1 Mafumu 10:2 nkhani