18 Ndipo anacoka ku Midyani nafika ku Parani, natenga anthu a ku Parani pamodzi nao, nafika ku Aigupto kwa Farao mfumu ya Aigupto, ameneyo anampatsa nyumba, namnenera zakudya, nampatsako dziko.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 11
Onani 1 Mafumu 11:18 nkhani