1 Mafumu 13:11 BL92

11 Ndipo ku Beteli kunakhala mneneri wokalamba, ndipo mwana wace wina anadzamfotokozera macitidwe onse anawacita munthu wa Mulunguyo tsiku lomwelo m'Beteli ndi mau ace anawanena ndi mfumu; inde omwe aja iwo anamfotokozera atate wao.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 13

Onani 1 Mafumu 13:11 nkhani