1 Mafumu 13:18 BL92

18 Ndipo anati kwa iye, Inenso ndine mneneri wonga iwe, ndipo mthenga analankhula ndi ine mwa mau a Yehova, nati, Kambwezere kwanu, kuti akadye mkate, namwe madzi. Koma anamnamiza.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 13

Onani 1 Mafumu 13:18 nkhani