1 Mafumu 14:15 BL92

15 Popeza Yehova adzawakantha Aisrayeli monga bango ligwedezeka ndi madzi, nadzazula Aisrayeli m'dziko lino labwino analipatsa makolo ao, nadzawamwazira ku tsidya lija la Firate, popeza iwo anapanga zifanizo zao zokwiyitsa Yehova.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 14

Onani 1 Mafumu 14:15 nkhani