1 Mafumu 14:6 BL92

6 Ndipo kunacitika, pamene Ahiya anamva mgugu wa mapazi ace alinkulowa pakhomo, anati, Lowa mkazi iwe wa Yerobiamu, wadzizimbaitsiranji? pakuti ine ndatumidwa kwa iwe ndi mau olasa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 14

Onani 1 Mafumu 14:6 nkhani