1 Mafumu 2:27 BL92

27 Motero Solomo anacotsa Abyatara asakhalenso wansembe wa Yehova, kuti akakwaniritse mau a Yehova amene aja adalankhula ku Silo za mbumba ya Eli.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 2

Onani 1 Mafumu 2:27 nkhani