1 Mafumu 2:36 BL92

36 Ndipo mfumu inatuma munthu kukaitana Simeyi, nati kwa iye, Udzimangire nyumba m'Yerusalemu, nukhale komweko osaturukako kumka kwina konse.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 2

Onani 1 Mafumu 2:36 nkhani